Yesaya 58:2 BL92

2 Koma iwo andifuna Ine tsiku ndi tsiku, ndi kukondwera kudziwa njira zanga; monga mtundu wa anthu ocita cilungamo, osasiya cilangizo ca Mulungu wao, iwo andipempha Ine zilangizo zolungama, nakondwerera kuyandikira kwa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 58

Onani Yesaya 58:2 nkhani