Yesaya 61:9 BL92

9 Ndipo ana ao adzadziwidwa mwa amitundu, ndi obadwa ao mwa anthu; onse amene awaona adzawazindikira kuti iwo ndiwo ana amene Yehova wadalitsa.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 61

Onani Yesaya 61:9 nkhani