Yesaya 62:8 BL92

8 Yehova analumbira pa dzanja lace lamanja, ndi mkono wace wamphamvu, Zoonadi, sindidzaperekanso tirigu wako akhale cakudya ca adani ako, ndipo alendo sadzamwa vinyo wako amene iwe unagwirira nchito;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 62

Onani Yesaya 62:8 nkhani