Yesaya 65:13 BL92

13 Cifukwa cace atero Ambuye Yehova, Taonani atumiki anga adzadya, koma inu mudzakhala ndi njala; taonani, atumiki anga adzamwa, koma inu mudzakhala ndi ludzu; taonani, atumiki anga adzasangalala, koma inu mudzakhala ndi manyazi;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 65

Onani Yesaya 65:13 nkhani