8 Ndipo iye adzapitapitakulowa m'Yuda; adzasefukira, napitirira; adzafikira m'khosi; ndi kutambasula kwa mapiko ace, kudzakwanira dziko lanu m'citando mwace, inu Imanueli.
Werengani mutu wathunthu Yesaya 8
Onani Yesaya 8:8 nkhani