Yesaya 8:9 BL92

9 Citani phokoso, anthu inu, koma mudzatyokatyoka; cherani khutu, inu nonse a maiko akutari; kwindani nokha, koma mudzatyokatyoka; kwindani nokha, koma mudzatyokatyoka.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 8

Onani Yesaya 8:9 nkhani