Yesaya 26:10 BL92

10 Ungayanje woipa, koma sadzaphunzira cilungamo; m'dziko la macitidwe oongoka, iye adzangocimwa, sadzaona cifumu ca Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 26

Onani Yesaya 26:10 nkhani