Yesaya 41:2 BL92

2 Ndani anautsa wina wocokera kum'mawa, amene amuitana m'cilungamo, afike pa phazi lace? Iye apereka amitundu patsogolo pace, namlamuliritsa mafumu; nawapereka monga pfumbi ku lupanga lace, monga ciputu couluzidwa ku uta wace.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 41

Onani Yesaya 41:2 nkhani