1 Mulungu wa cilemekezo canga, musakhale cete;
2 Pakuti pakamwa pa woipa ndi pakamwa pa cinyengo pananditsegukira;Anandilankhulira ndi m'kamwa mwa bodza.
3 Ndipo anandizinga ndi mau a udani,Nalimbana nane kopanda cifukwa.
4 M'malo mwa cikondi canga andibwezera udani;Koma ine, kupemphera ndiko.