22 Cosiyira ca kwa Israyeli mtumiki wace;Pakuti cifundo cace ncosatha.
23 Amene anatikumbukila popepuka ife;Pakuti cifundo cace ncosatha.
24 Natikwatula kwa otisautsa;Pakuti cifundo cace ncosatha.
25 Ndiye wakupatsa nyama zonse cakudya;Pakuti cifundo cace ncosatha.
26 Yamikani Mulungu wa kumwamba,Pakuti cifundo cace ncosatha.