Masalmo 17:14 BL92

14 Kwa anthu, ndi dzanja lanu, Yehova,Kwa anthu a dziko lapansi pano amene colowa cao ciri m'moyo uno,Ndipo mimba yao muidzaza ndi cuma canu cobisika:Akhuta mtima ndi ana,Nasiyira ana amakanda zocuruka zao.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 17

Onani Masalmo 17:14 nkhani