15 Maso a Yehova ali pa olungama mtima,Ndipo makutu ace achereza kulira kwao.
16 Nkhopeya Yehovaitsutsananao akucita zoipa,Kudula cikumbukilo cao pa dziko lapansi.
17 Iwowo anaitana, ndipo Yehova anawamva,Nawalanditsa ku masautso ao onse.
18 Yehova ali pafupi ndi iwo a mtimawosweka,Apulumutsa iwo a mzimu wolapadi,
19 Masautso a wolungama mtima acuruka:Koma Yehova amlanditsa mwa onsewa.
20 Iye asunga mafupa ace onse:Silinatyoka limodzi lonse.
21 Mphulupulu idzamupha woipa:Ndipo adzawatsutsa kumlandu iwo akudana naye wolungama.