Masalmo 35:10 BL92

10 Mafupa anga onse adzanena, Yehova, afanana ndi Inu ndani,Wakulanditsa wozunzika kwa iye amene amposa mphamvu,Ndi wozunzika ndi waumphawi kwa iye amfunkhira?

Werengani mutu wathunthu Masalmo 35

Onani Masalmo 35:10 nkhani