Masalmo 75:8 BL92

8 Pakuti m'dzanja la Yehova muli cikho;Ndi vinyo wace acita thobvu;Cidzala ndi zosanganizira, ndipo atsanulako:Indedi, oipa onse a pa dziko lapansi adzamwaNadzagugudiza nsenga zace.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 75

Onani Masalmo 75:8 nkhani