Masalmo 35:26 BL92

26 Acite manyazi, nadodome iwo akukondwera cifukwa ca coipa cidandigwera:Abvekeke ndi manyazi ndi kupunzika iwo akudzikuza pa ine.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 35

Onani Masalmo 35:26 nkhani